Masalimo 119:132 - Buku Lopatulika132 Munditembenukire, ndi kundichitira chifundo, monga mumatero nao akukonda dzina lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014132 Munditembenukire, ndi kundichitira chifundo, monga mumatero nao akukonda dzina lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa132 Yang'aneni, ndipo mundikomere mtima monga m'mene mumachitira ndi anthu okukondani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero132 Tembenukirani kwa ine ndipo mundichitire chifundo, monga mumachitira nthawi zonse kwa iwo amene amakonda dzina lanu. Onani mutuwo |