Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 119:12 - Buku Lopatulika

12 Inu ndinu wodala Yehova; ndiphunzitseni malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Inu ndinu wodala Yehova; ndiphunzitseni malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Mutamandike, Inu Chauta, phunzitseni malamulo lanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Mutamandike Inu Yehova; phunzitseni malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:12
17 Mawu Ofanana  

Landirani, Yehova, zopereka zaufulu za pakamwa panga, ndipo ndiphunzitseni maweruzo anu.


Muchitire mtumiki wanu monga mwa chifundo chanu, ndipo ndiphunzitseni malemba anu.


Muwalitse nkhope yanu pa mtumiki wanu; ndipo mundiphunzitse malemba anu.


Mundiphunzitse, Yehova, njira ya malemba anu; ndidzaisunga kufikira kutha kwake.


Dziko lapansi lidzala nacho chifundo chanu, Yehova; mundiphunzitse malemba anu.


Mundiphunzitse chisiyanitso ndi nzeru; pakuti ndinakhulupirira malamulo anu.


Inu ndinu wabwino, ndi wakuchita zabwino; mundiphunzitse malemba anu.


Mundiphunzitse chokonda Inu; popeza Inu ndinu Mulungu wanga; Mzimu wanu ndi wokoma; munditsogolere kuchidikha.


Mundionetse njira yanu, Yehova; ndidzayenda m'choonadi chanu, muumbe mtima wanga ukhale umodzi kuti uliope dzina lanu.


Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo;


Koma Nkhosweyo, Mzimu Woyera, amene Atate adzamtuma m'dzina langa, Iyeyo adzaphunzitsa inu zonse, nadzakumbutsa inu zinthu zonse zimene ndinanena kwa inu.


monga mwa Uthenga Wabwino wa ulemerero wa Mulungu wolemekezeka, umene anandisungitsa ine.


limene adzalionetsa m'nyengo za Iye yekha, amene ali Mwini Mphamvu wodala ndi wayekha, ndiye Mfumu ya mafumu ndi Mbuye wa ambuye;


Ndipo inu, kudzoza kumene munalandira kuchokera kwa Iye, kukhala mwa inu, ndipo simusowa kuti wina akuphunzitseni; koma monga kudzoza kwake kukuphunzitsani za zinthu zonse, ndipo kuli koona, sikuli bodza ai, ndipo monga kudaphunzitsa inu, mukhale mwa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa