Masalimo 119:11 - Buku Lopatulika11 Ndinawabisa mau anu mumtima mwanga, kuti ndisalakwire Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndinawabisa mau anu mumtima mwanga, kuti ndisalakwire Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndasunga mau anu mumtima mwanga, kuti ndisakuchimwireni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndasunga mawu anu mu mtima mwanga kuti ndisakuchimwireni. Onani mutuwo |