Masalimo 119:105 - Buku Lopatulika105 Mau anu ndiwo nyali ya ku mapazi anga, ndi kuunika kwa panjira panga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014105 Mau anu ndiwo nyali ya ku mapazi anga, ndi kuunika kwa panjira panga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa105 mau anu ndiye nyale ya mapazi anga, ndipo amaunikira njira yanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero105 Mawu anu ndi nyale ya kumapazi kwanga ndi kuwunika kwa pa njira yanga. Onani mutuwo |