Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:101 - Buku Lopatulika

101 Ndinaletsa mapazi anga njira iliyonse yaoipa, kuti ndisamalire mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

101 Ndinaletsa mapazi anga njira iliyonse yaoipa, kuti ndisamalire mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

101 Ndimaletsa miyendo yanga kuti isayende m'njira yoipa iliyonse, kuti choncho ndizisunga mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

101 Ndimaletsa miyendo yanga kuyenda mʼnjira iliyonse yoyipa kuti ndithe kumvera mawu anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:101
12 Mawu Ofanana  

Malangizo anu andizindikiritsa; chifukwa chake ndidana nao mayendedwe onse achinyengo.


Yafika nyengo yakuti Yehova achite kanthu; pakuti anaswa chilamulo chanu.


Odala iwo akusunga mboni zake, akumfuna ndi mtima wonse;


Ndipo ndinakhala wangwiro ndi Iye, ndipo ndinadzisunga wosachita choipa changa.


Mwananga, usayende nao m'njira; letsa phazi lako ku mayendedwe ao;


Tonse tasochera ngati nkhosa; tonse tayenda yense m'njira ya mwini yekha; ndipo Yehova anaika pa Iye mphulupulu ya ife tonse.


woipa asiye njira yake, ndi munthu wosalungama asiye maganizo ake, nabwere kwa Yehova; ndipo Yehova adzamchitira chifundo; ndi kwa Mulungu wathu, pakuti Iye adzakhululukira koposa.


Bwanji uyendayenda kwambiri ndi kusintha njira yako? Udzachitanso manyazi ndi Ejipito monga unachita manyazi ndi Asiriya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa