Masalimo 119:100 - Buku Lopatulika100 Ndizindikira koposa okalamba popeza ndinasunga malangizo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014100 Ndizindikira koposa okalamba popeza ndinasunga malangizo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa100 Ndili ndi nzeru kupambana okalamba, pakuti ndimatsata malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero100 Ndili ndi nzeru zochuluka zomvetsera zinthu kuposa anthu okalamba, popeza ndimamvera malangizo anu. Onani mutuwo |