Masalimo 119:10 - Buku Lopatulika10 Ndinakufunani ndi mtima wanga wonse; ndisasokere kusiyana nao malamulo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndinakufunani ndi mtima wanga wonse; ndisasokere kusiyana nao malamulo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndimakufunafunani ndi mtima wanga wonse, musalole kuti ndisiye kumvera malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndimakufunafunani ndi mtima wanga wonse; musalole kuti ndisochere kuchoka pa malamulo anu. Onani mutuwo |