Masalimo 116:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti munalanditsa moyo wanga kuimfa, maso anga kumisozi, mapazi anga, ndingagwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti munalanditsa moyo wanga kuimfa, maso anga kumisozi, mapazi anga, ndingagwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pakuti Inu Chauta, mwandipulumutsa ku imfa, mwaletsa misozi yanga, mwanditeteza kuti ndisaphunthwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa, maso anga ku misozi, mapazi anga kuti angapunthwe, Onani mutuwo |