Masalimo 116:6 - Buku Lopatulika6 Yehova asunga opusa; ndidafooka ine, koma anandipulumutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Yehova asunga opusa; ndidafooka ine, koma anandipulumutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chauta amasunga a mtima wodzichepetsa. Pamene ndidagwa m'zoopsa, Iye adandipulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima; pamene ndinali ndi chosowa chachikulu, Iye anandipulumutsa. Onani mutuwo |