Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 116:18 - Buku Lopatulika

18 Ndidzachita zowinda zanga za kwa Yehova, tsopano, pamaso pa anthu ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndidzachita zowinda zanga za kwa Yehova, tsopano, pamaso pa anthu ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ndidzachita zimene ndidalumbira kwa Chauta pamaso pa anthu ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 116:18
6 Mawu Ofanana  

Ndidzachita zowinda zanga za kwa Yehova, tsopano, pamaso pa anthu ake onse.


Lemekezo langa lidzakhala la Inu mu msonkhano waukulu, zowinda zanga ndidzazichita pamaso pa iwo akumuopa Iye.


Ozunzika adzadya nadzakhuta, adzayamika Yehova iwo amene amfuna, ukhale moyo mtima wako nthawi zonse.


Wakumva pemphero Inu, zamoyo zonse zidzadza kwa Inu.


Windani ndipo chitirani Yehova Mulungu wanu zowindazo; onse akumzinga abwere nacho chopereka cha kwa Iye amene ayenera kumuopa.


Kusawinda kupambana kuwinda osachita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa