Masalimo 116:11 - Buku Lopatulika11 Pofulumizidwa mtima ndinati ine, anthu onse nga mabodza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pofulumizidwa mtima ndinati ine, anthu onse nga mabodza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pamene ndinkachita mantha, ndidati, “Anthu ndi osakhulupirika.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati, “Anthu onse ndi abodza.” Onani mutuwo |