Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 115:16 - Buku Lopatulika

16 Kunena za kumwamba, kumwamba ndiko kwa Yehova; koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Kunena za kumwamba, kumwamba ndiko kwa Yehova; koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Kumwamba nkwa Chauta, koma dziko lapansi adapatsa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Kumwamba ndi kwa Yehova, koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 115:16
14 Mawu Ofanana  

Weramutsani thambo lanu, Yehova, nimutsike: Khudzani mapiri ndipo adzafuka.


Mlemekezeni, m'mwambamwamba, ndi madzi inu, a pamwamba pa thambo.


Munamchititsa ufumu pa ntchito za manja anu; mudagonjetsa zonse pansi pa mapazi ake;


Kumwamba ndi kwanu, dziko lapansi lomwe ndi lanu; munakhazika dziko lokhalamo anthu ndi kudzala kwake.


Munalenga kumpoto ndi kumwera; Tabori ndi Heremoni afuula mokondwera m'dzina lanu.


Pakuti atero Yehova amene analenga kumwamba, Iye ndiye Mulungu amene anaumba dziko lapansi, nalipanga; Iye analikhazikitsa, sanalilenge mwachabe; Iye analiumba akhalemo anthu; Ine ndine Yehova; ndipo palibenso wina.


Atero Yehova, Kumwamba ndi mpando wanga wachifumu, ndi dziko lapansi ndi choikapo mapazi anga; mudzandimangira Ine nyumba yotani? Ndi malo ondiyenera kupumamo ali kuti?


mudzawalondola mokwiya ndi kuwaononga pansi pa thambo la Yehova.


M'nyumba ya Atate wanga alimo malo okhalamo ambiri. Ngati sikudali kutero, ndikadakuuzani inu; pakuti ndipita kukukonzerani inu malo.


Taonani thambo, ndi kumwambamwamba, dziko lapansi, ndi zonse zili m'mwemo ndi zake za Yehova Mulungu wanu.


Pamene Wam'mwambamwamba anagawira amitundu cholowa chao, pamene anagawa ana a anthu, anaika malire a mitundu ya anthu, monga mwa kuwerenga kwao kwa ana a Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa