Masalimo 115:16 - Buku Lopatulika16 Kunena za kumwamba, kumwamba ndiko kwa Yehova; koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Kunena za kumwamba, kumwamba ndiko kwa Yehova; koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Kumwamba nkwa Chauta, koma dziko lapansi adapatsa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kumwamba ndi kwa Yehova, koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu. Onani mutuwo |