Masalimo 115:14 - Buku Lopatulika14 Yehova akuonjezereni dalitso, inu ndi ana anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Yehova akuonjezereni dalitso, inu ndi ana anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chauta akudalitseni inu, pamodzi ndi zidzukulu zanu zomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yehova akuwonjezereni madalitso; inuyo pamodzi ndi ana anu. Onani mutuwo |