Masalimo 114:8 - Buku Lopatulika8 amene anasanduliza thanthwe likhale thawale lamadzi, nsangalabwi ikhale kasupe wamadzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 amene anasanduliza thanthwe likhale thawale lamadzi, nsangalabwi ikhale kasupe wamadzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Iye amasandutsa thanthwe kukhala dziŵe lamadzi, amasandutsa mwala wolimba kukhala kasupe wa madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi. Onani mutuwo |