Masalimo 114:7 - Buku Lopatulika7 Unjenjemere, dziko lapansi iwe, pamaso pa Ambuye, pamaso pa Mulungu wa Yakobo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Unjenjemere, dziko lapansi iwe, pamaso pa Ambuye, pamaso pa Mulungu wa Yakobo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Njenjemera iwe dziko lapansi, chifukwa Chauta akubwera, zoonadi, akubwera Mulungu wa Yakobe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo, Onani mutuwo |