Masalimo 114:6 - Buku Lopatulika6 Munatumphatumphiranji ngati nkhosa zamphongo, mapiri inu? Ngati anaankhosa, zitunda inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Munatumphatumphiranji ngati nkhosa zamphongo, mapiri inu? Ngati anaankhosa, zitunda inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Inu mapiri, chikukuvutani nchiyani, kuti muzilumphalumpha ngati nkhosa zamphongo? Nanga inu zitunda, mukulumphiranji ngati anaankhosa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa? Onani mutuwo |