Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 114:5 - Buku Lopatulika

5 Unathawanji nawe, nyanja iwe? Unabwereranji m'mbuyo, Yordani iwe?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Unathawanji nawe, nyanja iwe? Unabwereranji m'mbuyo, Yordani iwe?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Iwe nyanja, chikukuvuta nchiyani kuti uzithaŵa? Nanga iwe Yordani, ukubwerereranji m'mbuyo?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 114:5
2 Mawu Ofanana  

Kodi Yehova anaipidwa nayo mitsinje? Mkwiyo wanu unali pamitsinje kodi, kapena ukali wanu panyanja, kuti munayenda pa akavalo anu, pa magaleta anu a chipulumutso?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa