Masalimo 111:4 - Buku Lopatulika4 Anachita chokumbukitsa zodabwitsa zake; Yehova ndiye wachisomo ndi nsoni zokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Anachita chokumbukitsa zodabwitsa zake; Yehova ndiye wachisomo ndi nsoni zokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amatikumbutsa ntchito zake zodabwitsa, Chauta ndi wokoma ndi wachifundo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike; Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo. Onani mutuwo |