Masalimo 108:13 - Buku Lopatulika13 Mwa Mulungu tidzachita molimbika mtima: Ndipo Iye adzapondereza otisautsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mwa Mulungu tidzachita molimbika mtima: Ndipo Iye adzapondereza otisautsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mulungu akakhala nafe, tidzamenya nkhondo molimba mtima, pakuti ndiye amene adzapondereza adani athu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano, ndipo adzapondereza pansi adani athu. Onani mutuwo |