Masalimo 107:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti akhutitsa mtima wolakalaka, nadzaza mtima wanjala ndi zabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti akhutitsa mtima wolakalaka, nadzaza mtima wanjala ndi zabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chauta amapha ludzu la munthu womva ludzu, amamudyetsa zinthu zabwino munthu womva njala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 pakuti Iye wapha ludzu la munthu womva ludzu ndipo wakhutitsa wanjala ndi zinthu zabwino. Onani mutuwo |