Masalimo 107:6 - Buku Lopatulika6 Pamenepo anafuulira kwa Yehova mumsauko mwao, ndipo anawalanditsa m'kupsinjika kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pamenepo anafuulira kwa Yehova mumsauko mwao, ndipo anawalanditsa m'kupsinjika kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono anthu aja adalira kwa Chauta pamene anali m'mavuto amenewo, ndipo Chauta adaŵapulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamenepo analirira Yehova mʼmavuto awo ndipo Iye anawapulumutsa ku masautso awo. Onani mutuwo |