Masalimo 107:5 - Buku Lopatulika5 Anamva njala ndi ludzu, moyo wao unakomoka m'kati mwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anamva njala ndi ludzu, moyo wao unakomoka m'kati mwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adamva njala ndi ludzu, moyo wao unkafookeratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iwo anamva njala ndi ludzu, ndipo miyoyo yawo inafowokeratu. Onani mutuwo |