Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 107:5 - Buku Lopatulika

5 Anamva njala ndi ludzu, moyo wao unakomoka m'kati mwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Anamva njala ndi ludzu, moyo wao unakomoka m'kati mwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Adamva njala ndi ludzu, moyo wao unkafookeratu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Iwo anamva njala ndi ludzu, ndipo miyoyo yawo inafowokeratu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 107:5
9 Mawu Ofanana  

ndi uchi ndi mafuta, ndi nkhosa, ndi mase a ng'ombe, kuti adye Davide, ndi anthu amene anali naye; pakuti anati, Anthu ali ndi njala, olema, ndi aludzu m'chipululumo.


nanena nao ana a Israele, Ha? Mwenzi titafa ndi dzanja la Yehova m'dziko la Ejipito, pokhala ife pa miphika ya nyama, pakudya mkate ife chokhuta; pakuti mwatitulutsa kudza nafe m'chipululu muno kudzapha msonkhano uwu wonse ndi njala.


Ndipo pomwepo anthu anamva ludzu lokhumba madzi; ndi anthu anadandaulira Mose, nati, Munatikwezeranji kuchokera ku Ejipito, kudzatipha ife ndi ana athu ndi zoweta zathu ndi ludzu?


Wachipala achita zake ndi nsompho, nagwira ntchito ndi makala, nafanizira fanolo ndi nyundo, nagwira ntchito yake ndi mkono wake wamphamvu; inde, ali ndi njala, ndipo mphamvu zake zilephera; iye samwa madzi, nalefuka.


Ndikatulukira kumunda, taonani ophedwa ndi lupanga! Ndikalowa m'mzinda, taonani odwala ndi njala! Pakuti mneneri ndi wansembe ayendayenda m'dziko osadziwa kanthu.


Tauka, tafuula usiku, poyamba kulonda; tsanulira mtima wako ngati madzi pamaso pa Ambuye; takwezera maso ako kwa Iye, chifukwa cha moyo wa tiana tako, timene tilefuka ndi njala pa malekezero a makwalala onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa