Masalimo 107:41 - Buku Lopatulika41 Koma aika waumphawi pamsanje posazunzika, nampatsa mabanja ngati gulu la nkhosa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Koma aika waumphawi pamsanje posazunzika, nampatsa mabanja ngati gulu la nkhosa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Koma anthu osoŵa adaŵatulutsa m'mavuto ao, adachulukitsa mabanja ao ngati magulu a nkhosa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Koma Iyeyo anakweza anthu osowa kuchoka ku masautso awo ngati magulu a nkhosa. Onani mutuwo |