Masalimo 107:3 - Buku Lopatulika3 nawasokolotsa kumaiko, kuchokera kum'mawa ndi kumadzulo, kumpoto ndi kunyanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nawasokolotsa kumaiko, kuchokera kum'mawa ndi kumadzulo, kumpoto ndi kunyanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Waŵasonkhanitsa kuchokera ku maiko onse, kuchokera kuvuma ndi kuzambwe, kumpoto ndi kumwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 iwo amene anawasonkhanitsa kuchokera ku mayiko, kuchokera kumadzulo ndi kummawa, kuchokera kumpoto ndi kummwera. Onani mutuwo |