Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 107:16 - Buku Lopatulika

16 Popeza adaswa zitseko zamkuwa, nathyola mipiringidzo yachitsulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Popeza adaswa zitseko zamkuwa, nathyola mipiringidzo yachitsulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Pajatu adathyola zitseko zamkuŵa, nadula paŵiri mipiringidzo yachitsulo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 pakuti Iye amathyola zipata zamkuwa ndi kudula pakati mipiringidzo yachitsulo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 107:16
3 Mawu Ofanana  

Wothyola wakwera pamaso pao; iwo anathyola, napita kuchipata, natuluka pomwepo; ndi mfumu yao yapita pamaso pao, ndipo Yehova awatsogolera.


Koma Samisoni anagona mpaka pakati pa usiku, nauka pakati pa usiku, nagwira zitseko za pa chipata cha mzinda, ndi mphuthu ziwirizo, nazichotsa ndi mpiringidzo womwe, naziika pa mapewa ake, nakwera nazo pamwamba paphiri lili pandunji pa Hebroni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa