Masalimo 107:11 - Buku Lopatulika11 popeza anapikisana nao mau a Mulungu, napeputsa uphungu wa Wam'mwambamwamba; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 popeza anapikisana nao mau a Mulungu, napeputsa uphungu wa Wam'mwambamwamba; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 pakuti adaatsutsa mau a Mulungu, adaakana monyoza malangizo a Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 pakuti iwowo anawukira mawu a Mulungu ndi kunyoza uphungu wa Wammwambamwamba. Onani mutuwo |