Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 107:11 - Buku Lopatulika

11 popeza anapikisana nao mau a Mulungu, napeputsa uphungu wa Wam'mwambamwamba;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 popeza anapikisana nao mau a Mulungu, napeputsa uphungu wa Wam'mwambamwamba;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 pakuti adaatsutsa mau a Mulungu, adaakana monyoza malangizo a Wopambanazonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 pakuti iwowo anawukira mawu a Mulungu ndi kunyoza uphungu wa Wammwambamwamba.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 107:11
23 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova analankhula ndi Manase ndi anthu ake, koma sanasamalire.


koma ananyodola mithenga ya Mulungu, napeputsa mau ake, naseka aneneri ake, mpaka ukali wa Yehova unaukira anthu ake, mpaka panalibe cholanditsa.


Iye anawalanditsa kawirikawiri; koma anapikisana ndi Iye mwa uphungu wao, ndi mphulupulu zao zinawafoketsa.


Makolo athu sanadziwitse zodabwitsa zanu mu Ejipito; sanakumbukire zachifundo zanu zaunyinji; koma anapikisana ndi Inu kunyanja, ku Nyanja Yofiira.


Mboni zanu zomwe ndizo zondikondweretsa, ndizo zondipangira nzeru.


Munakwera kunka kumwamba, munapita nao undende kuuyesa ndende; munalandira zaufulu mwa anthu, ngakhale mwa opikisana nanu, kuti Yehova Mulungu akakhale nao.


Mulungu amangitsira banja anthu a pa okha; atulutsa am'ndende alemerere; koma opikisana naye akhala m'dziko lopanda madzi.


Mudzanditsogolera ndi uphungu wanu, ndipo mutatero, mudzandilandira mu ulemerero.


Kawirikawiri nanga anapikisana ndi Iye kuchigwako, nammvetsa chisoni m'chipululu.


koma munapeputsa uphungu wanga wonse, ndi kukana kudzudzula kwanga.


amene ati, Mlekeni iye akangaze, mlekeni iye afulumize ntchito yake kuti ife tione; ndipo lekani uphungu wa Woyera wa Israele uyandikire, udze kuti tiudziwe!


Koma mau amene wanena ndi ife m'dzina la Yehova, sitidzakumvera iwe.


Koma Afarisi, ndiwo okonda ndalama, anamva izi zonse; ndipo anamseka.


Koma Afarisi ndi achilamulo anakaniza uphungu wa Mulungu kwa iwo okha, popeza sanabatizidwe ndi iye.


Pakuti sindinakubisirani pakukulalikirani uphungu wonse wa Mulungu.


Ndipo monga iwo anakana kukhala naye Mulungu m'chidziwitso chao, anawapereka Mulungu kumtima wokanika, kukachita zinthu zosayenera;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa