Masalimo 107:10 - Buku Lopatulika10 Iwo akukhala mumdima ndi mu mthunzi wa imfa, omangika ndi kuzunzika ndi chitsulo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Iwo akukhala mumdima ndi mu mthunzi wa imfa, omangika ndi kuzunzika ndi chitsulo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ena adakhala mu mdima ali ndi chisoni, anali am'ndende ozunzika m'maunyolo achitsulo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ena anakhala mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu, amʼndende ovutika mʼmaunyolo achitsulo, Onani mutuwo |