Masalimo 107:1 - Buku Lopatulika1 Yamikani Yehova pakuti Iye ndiye wabwino; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yamikani Yehova pakuti Iye ndiye wabwino; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Thokozani Chauta chifukwa ngwabwino, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino; pakuti chikondi chake ndi chosatha. Onani mutuwo |
Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;