Masalimo 106:8 - Buku Lopatulika8 Koma anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake, kuti adziwitse chimphamvu chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake, kuti adziwitse chimphamvu chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Komabe Iye adaŵapulumutsa malinga ndi ulemerero wa dzina lake, kuti aonetse mphamvu zake zazikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Komabe Iye anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake, kuti aonetse mphamvu zake zazikulu. Onani mutuwo |