Masalimo 106:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo anawapereka m'manja a amitundu; ndipo odana nao anachita ufumu pa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo anawapereka m'manja a amitundu; ndipo odana nao anachita ufumu pa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Adaŵapereka kwa mitundu ina ya anthu, kotero kuti amene ankadana nawo, ndiwo amene ankaŵalamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Iye anawapereka kwa anthu a mitundu ina, ndipo adani awo anawalamulira. Onani mutuwo |