Masalimo 106:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anawapulumutsa m'dzanja la iye amene anawada, nawaombola kudzanja la mdani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anawapulumutsa m'dzanja la iye amene anawada, nawaombola kudzanja la mdani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Motero adaŵapulumutsa kwa amaliwongo, naŵalanditsa ku mphamvu za adani ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anawapulumutsa mʼdzanja la amaliwongo; anawawombola mʼdzanja la mdani. Onani mutuwo |