Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 104:22 - Buku Lopatulika

22 Potuluka dzuwa, zithawa, zigona pansi m'ngaka mwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Potuluka dzuwa, zithawa, zigona pansi m'ngaka mwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Dzuŵa likamatuluka, imabwerera nkukagona m'mapanga mwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Dzuwa limatuluka ndipo iyo imapita kukabisala; imabwerera kukagona pansi mʼmapanga awo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:22
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo zilombo zilowa mobisalamo, ndipo zikhala m'ngaka mwao.


Ovala korona ako akunga dzombe, ndi akazembe, ndi akazembe ako ngati ziwalamsatsi zakutera m'matchinga tsiku lachisanu, koma likatuluka dzuwa ziuluka ndi kuthawa, ndi kumene zinakhalako sikudziwikanso.


Pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika, ndipo sakudza kwa kuunika, kuti zingatsutsidwe ntchito zake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa