Masalimo 104:21 - Buku Lopatulika21 Misona ya mkango ibangula potsata nyama yao, nifuna chakudya chao kwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Misona ya mkango ibangula potsata nyama yao, nifuna chakudya chao kwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Misona ya mikango imabangula pofunafuna nyama, kupempha chakudya kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mikango imabangula kufuna nyama, ndi kufunafuna chakudya chawo kuchokera kwa Mulungu. Onani mutuwo |