Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 104:18 - Buku Lopatulika

18 Mapiri aatali ndiwo ayenera zinkhoma; pamatanthwe mpothawirapo mbira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Mapiri atali ndiwo ayenera zinkhoma; pamatanthwe mpothawirapo mbira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 M'mapiri aatali ndimo m'mene mumakhala mbalale, m'matanthwe ndimo m'mene mumathaŵira mbira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mapiri ataliatali ndi a mbalale; mʼmingʼalu ya miyala ndi mobisalamo mbira.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 104:18
5 Mawu Ofanana  

Kodi udziwa nyengo yakuswana zinkhoma? Kodi wapenyerera pakuswa mbawala?


Mbira ndi mtundu wopanda mphamvu, koma ziika nyumba zao m'matanthwe.


Ndi mbira, ingakhale ibzikula koma yosagawanika chiboda, muiyese yodetsedwa.


Koma izi zokha simuyenera kuzidya mwa zobzikulazo, kapena zogawanika chiboda: ngamira, ndi kalulu, ndi mbira, popeza zibzikula, koma zosagawanika chiboda, muziyese zodetsa;


Tsono Saulo anatenga anthu zikwi zitatu osankhika pakati pa Aisraele onse, namuka, kukafuna Davide ndi anthu ake m'matanthwe a zinkhoma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa