Masalimo 104:17 - Buku Lopatulika17 m'mwemo mbalame zimanga zisa zao; pokhala chumba mpa mitengo ya mikungudza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 m'mwemo mbalame zimanga zisa zao; pokhala chumba mpa mitengo ya mikungudza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mbalame zimamanga zisa m'menemo, dokowe amamanga chisa m'mikungudzamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mbalame zimamanga zisa zawo; kakowa ali ndi malo ake mʼmikungudzamo. Onani mutuwo |