Masalimo 104:16 - Buku Lopatulika16 Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mitengo ya Chauta amaithirira ndi madzi ambiri, mikungudza ya ku Lebanoni imene adaibzala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Mitengo ya Yehova ndi yothiriridwa bwino, mikungudza ya ku Lebanoni imene Iye anadzala. Onani mutuwo |