Masalimo 104:14 - Buku Lopatulika14 Ameretsa msipu ziudye ng'ombe, ndi zitsamba achite nazo munthu; natulutse chakudya chochokera m'nthaka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ameretsa msipu ziudye ng'ombe, ndi zitsamba achite nazo munthu; natulutse chakudya chochokera m'nthaka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mumameretsa udzu kuti ng'ombe zidye, ndi zomera kuti munthu azilima ndi kupeza chakudya m'nthaka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Amameretsa udzu kuti ngʼombe zidye, ndi zomera, kuti munthu azilima kubweretsa chakudya kuchokera mʼdziko lapansi: Onani mutuwo |