Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 9:49 - Buku Lopatulika

49 Pakuti onse adzathiridwa mchere wamoto.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Pakuti onse adzathiridwa mchere wamoto.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 “Onse adzayeretsedwa ndi moto monga momwe nsembe imayeretsedwa ndi mchere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Aliyense adzayesedwa ndi moto.

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:49
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ubwere nazo kwa Yehova, ndi ansembe athirepo mchere, ndi kuzipereka nsembe yopsereza ya Yehova.


Ndipo chopereka chako chilichonse cha nsembe yaufa uzichikoleretsa ndi mchere; usasowe mchere wa chipangano cha Mulungu wako pa nsembe yako yaufa; pa zopereka zako zonse uzipereka mchere.


Inu ndinu mchere wa dziko lapansi; koma mcherewo ngati ukasukuluka, adzaukoleretsa ndi chiyani? Pamenepo sungakwanirenso kanthu konse, koma kuti ukaponyedwe kunja, nupondedwe ndi anthu.


kumeneko mphutsi yao siikufa, ndi moto suzimidwa.


Mchere uli wabwino; koma ngati mchere unasukuluka, mudzaukoleretsa ndi chiyani? Khalani nao mchere mwa inu nokha, ndipo khalani ndi mtendere wina ndi mnzake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa