Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 9:40 - Buku Lopatulika

40 Pakuti iye wosatsutsana ndi ife athandizana nafe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Pakuti iye wosatsutsana ndi ife athandizana nafe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Chifukwa wosatsutsana nafe, ndi wogwirizana nafe ameneyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 pakuti aliyense amene satsutsana nafe ali mbali yathu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:40
3 Mawu Ofanana  

Iye wosakhala pamodzi ndi Ine akana Ine, ndi iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwazamwaza.


Koma Yesu anati, Musamamletsa iye; pakuti palibe munthu adzachita champhamvu m'dzina langa, nadzakhoza msanga kundinenera Ine zoipa.


Iye wosavomerezana ndi Ine atsutsana ndi Ine; ndipo iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwaza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa