Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 9:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Atatero adatenga mwana, namkhazika pakati pao nkumufungata, naŵauza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Anatenga kamwana nakayimiritsa pakati pawo ndipo anawawuza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:36
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,


Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.


Ndipo m'mene anakhala pansi anaitana khumi ndi awiriwo; nanena nao, Ngati munthu afuna kukhala woyamba, akhale wakuthungo wa onse, ndi mtumiki wa onse.


Munthu aliyense adzalandira kamodzi ka tiana totere chifukwa cha dzina langa, alandira Ine; ndipo yense amene akalandira Ine, salandira Ine, koma Iye amene anandituma Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa