Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 9:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo anachoka iwo kumeneko, napyola pakati pa Galileya; ndipo Iye sanafune kuti munthu adziwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo anachoka iwo kumeneko, napyola pakati pa Galileya; ndipo Iye sanafune kuti munthu adziwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Atachoka kumeneko, Yesu ndi ophunzira ake ankadutsa m'dziko la Galileya. Koma Iye sadafune kuti anthu adziŵe,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Anachoka malo amenewo nadutsa ku Galileya. Yesu sanafune kuti wina aliyense adziwe kumene anali,

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:30
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anati kwa iwo, Mtundu uwu sungathe kutuluka ndi kanthu kena konse, koma ndi kupemphera.


Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso mu Galileya,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa