Marko 9:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Iye anati kwa iwo, Mtundu uwu sungathe kutuluka ndi kanthu kena konse, koma ndi kupemphera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Iye anati kwa iwo, Mtundu uwu sukhoza kutuluka ndi kanthu kena konse, koma ndi kupemphera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Yesu adayankha kuti, “Mzimu wa mtundu umenewu, pokhapokha mutayamba mwapemphera mpamene mungautulutse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Iye anayankha kuti, “Mtundu uwu umatuluka pokhapokha mwapemphera ndi kusala kudya.” Onani mutuwo |