Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 9:27 - Buku Lopatulika

27 Koma Yesu anamgwira dzanja lake, namnyamutsa; ndipo anaimirira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Koma Yesu anamgwira dzanja lake, namnyamutsa; ndipo anaimirira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Koma Yesu adamugwira dzanja namdzutsa, mwanayo nkuimirira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Koma Yesu anamugwira dzanja ndipo anamuyimiritsa, ndipo anayimirira.

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:27
11 Mawu Ofanana  

Pakuti Ine Yehova Mulungu wako ndidzagwira dzanja lako lamanja, ndi kunena kwa iwe, Usaope ndidzakuthandiza iwe.


Koma pamene khamulo linatulutsidwa, Iye analowamo, nagwira dzanja lake; ndipo kabuthuko kadauka.


ndipo anadza namgwira dzanja, namuutsa; ndipo malungo anamleka, ndipo anawatumikira iwo.


Ndipo Yesu anagwidwa chifundo, natansa dzanja namkhudza iye, nanena naye, Ndifuna; khala wokonzedwa.


Ndipo anagwira dzanja lake la mwana, nanena kwa iye, Talita koumi, ndiko kunena posandulika, Buthu, ndinena ndi iwe, Uka.


Ndipo anamgwira dzanja munthu wakhunguyo, natulukira naye kunja kwa mudzi; ndipo atamthira malovu m'maso mwake, naika manja pa iye, anamfunsa, Uona kanthu kodi?


Ndipo pamene unafuula, numng'ambitsa, unatuluka; ndipo mwana anakhala ngati wakufa; kotero kuti ambiri ananena, Wamwalira.


Ndipo pamene Iye adalowa m'nyumba, ophunzira ake anamfunsa m'tseri, kuti, Nanga bwanji sitinathe ife kuutulutsa?


Ndipo kapitao wamkulu anamgwira dzanja, napita naye padera, namfunsa m'tseri, Chiyani ichi uli nacho kundifotokozera?


Ndipo anamgwira iye kudzanja lake lamanja, namnyamutsa; ndipo pomwepo mapazi ake ndi mfundo za kumapazi zinalimbikitsidwa.


Ndipo Petro anamgwira dzanja, namnyamutsa; ndipo m'mene adaitana oyera mtima ndi amasiye, anampereka iye wamoyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa