Marko 9:27 - Buku Lopatulika27 Koma Yesu anamgwira dzanja lake, namnyamutsa; ndipo anaimirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma Yesu anamgwira dzanja lake, namnyamutsa; ndipo anaimirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma Yesu adamugwira dzanja namdzutsa, mwanayo nkuimirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Koma Yesu anamugwira dzanja ndipo anamuyimiritsa, ndipo anayimirira. Onani mutuwo |