Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 8:37 - Buku Lopatulika

37 Pakuti munthu akapereka chiyani chosintha nacho moyo wake?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Pakuti munthu akapereka chiyani chosintha nacho moyo wake?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Munthu angalipire chiyani choti aombolere moyo wake?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Kapena nʼchiyani chomwe munthu angapereke chosinthana ndi moyo wake?

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:37
4 Mawu Ofanana  

Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake?


Pakuti yense wakuchita manyazi chifukwa cha Ine, ndi cha mau anga mu mbadwo uno wachigololo ndi wochimwa, Mwana wa Munthu adzachitanso manyazi chifukwa cha iyeyu, pamene Iye adzafika nao angelo ake oyera, mu ulemerero wa Atate wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa