Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 8:36 - Buku Lopatulika

36 Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Nanga ndiye kuti munthu wapindulanji atapata zonse za pansi pano, iyeyo nkutaya moyo wake?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Kodi munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi, koma ndi kutaya moyo wake?

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:36
17 Mawu Ofanana  

Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Khungu kulipa khungu, inde munthu adzapereka zonse ali nazo kuombola moyo wake.


Kodi munthu apindulira Mulungu? Koma wanzeru angodzipindulira yekha.


pakuti pomwalira iye sadzamuka nako kanthu kalikonse; ulemu wake sutsika naye kumtsata m'mbuyo.


Mwanena, Kutumikira Mulungu nkwa chabe; ndipo tapindulanji ndi kusunga udikiro wake, ndi kuyenda ovala zamaliro pamaso pa Yehova wa makamu?


Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake?


Pakuti yense wakufuna kupulumutsa moyo wake adzautaya; ndipo yense wakutaya moyo wake chifukwa cha Ine, ndi chifukwa cha Uthenga Wabwino, adzaupulumutsa.


Pakuti munthu akapereka chiyani chosintha nacho moyo wake?


Pakuti munthu apindulanji, akadzilemezera dziko lonse lapansi nadzitayapo, kapena kulipapo moyo wake?


Ndipo munali nazo zobala zanji nthawi ija, m'zinthu zimene muchita nazo manyazi tsopano? Pakuti chimaliziro cha zinthu izi chili imfa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa