Marko 8:36 - Buku Lopatulika36 Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Nanga ndiye kuti munthu wapindulanji atapata zonse za pansi pano, iyeyo nkutaya moyo wake? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Kodi munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi, koma ndi kutaya moyo wake? Onani mutuwo |