Marko 8:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo ananena, nati, Yohane Mbatizi; ndi ena, Eliya; koma ena, Mmodzi wa aneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo ananena, nati, Yohane Mbatizi; ndi ena, Eliya; koma ena, Mmodzi wa aneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Iwo adayankha kuti, “Ena amati ndinu Yohane Mbatizi, ena amati ndinu Eliya, enanso amati ndinu mmodzi mwa aneneri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Iwo anayankha kuti, “Ena amati Yohane Mʼbatizi; ena amati Eliya; ndipo enanso amati ndinu mmodzi wa aneneri.” Onani mutuwo |