Marko 7:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Yesu adalamula anzake a munthuyo kuti, “Musakauzetu wina aliyense zimenezi.” Koma ngakhale adaŵaletsa mwamphamvu choncho, iwo adanka nalengeza ndithu zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Yesu anawalamula kuti asawuze wina aliyense. Koma pamene anapitiriza kuwaletsa, iwo anapitiriza kuyankhula za izi. Onani mutuwo |