Marko 7:28 - Buku Lopatulika28 Koma iye anavomera nanena ndi Iye, Inde Ambuye; tingakhale tiagalu ta pansi pa gome tikudyako nyenyeswa za ana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Koma iye anavomera nanena ndi Iye, Ine Ambuye; tingakhale tiagalu ta pansi pa gome tikudyako nyenyeswa za ana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Apo maiyo adati, “Nzoonadi, Ambuye, koma suja ngakhale agalu omwe amakhala m'munsi mwa tebulo nkumadyako nyenyeswa zimene ataya ana?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Mayiyo anayankha kuti, “Inde Ambuye, koma ngakhale agalu amadya zomwe zimagwa pansi kuchokera pa tebulo la ana.” Onani mutuwo |