Marko 6:49 - Buku Lopatulika49 koma iwo, pamene anamuona alikuyenda panyanja, anayesa kuti ndi mzukwa, nafuula: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 koma iwo, pamene anamuona alikuyenda panyanja, anayesa kuti ndi mzukwa, nafuula: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Koma ophunzira aja, pomuwona akuyenda pa madzi, adaaganiza kuti ndi mzukwa, nayamba kukuwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 koma atamuona Iye akuyenda pa nyanja, anaganiza kuti anali mzukwa. Iwo anafuwula, Onani mutuwo |