Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 6:47 - Buku Lopatulika

47 Ndipo pofika madzulo ngalawa inali pakati pa nyanja, ndi Iye yekha pamtunda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Ndipo pofika madzulo ngalawa inali pakati pa nyanja, ndi Iye yekha pamtunda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 M'mene kunkayamba kuda, nkuti chombo chija chili pakati pa nyanja, Yesu ali yekha pa mtunda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Pofika madzulo, bwato linali pakati pa nyanja, ndipo Iye anali yekha pa mtunda.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:47
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Iye anawauza makamuwo, anakwera m'phiri pa yekha, kukapemphera: ndipo pamene panali madzulo, Iye anakhala kumeneko yekha.


Ndipo atalawirana nao, anachoka Iye, nalowa m'phiri kukapemphera.


Ndipo pakuwaona ali kuvutidwa ndi kupalasa, pakuti mphepo inadza nikomana nao, pa ulonda wachinai wa usiku Iye anadza kwa iwo, alikuyenda pamwamba pa nyanja; nati awapitirire;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa